Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

  1. Home   »  
  2. Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

 

NDI MISOZI, ndi chisoni,
Ndiliratu kwa Inu Yesu;
Ndi chifundo chandigwira,
Ndilira kutí ndili wanu

E! Kwa Inu, E! Kwa Inu!
Ndilira kuti ndili wanu.

Mbuye Yesu ndi Atate,
Mundiwona ndili wosowa;
Ndimasowa Mzimu wanu,
Kuinga zonse za mumtima.

Mtenderewo, wosanyenga,
Ndilira ine m’mtima mwanga;
Kundimvetsa chimwemwetu,
Ndilira ine m’mtima mwanga.

Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera Inu;
Koma lero ndamva kuti,
Muli mwini wake wa moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 827 Wonsewu usiku

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version