Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

  1. Home   »  
  2. Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

 

NDINASOKERA kutali,
Ndinadya ndi nguluwe,
Ndinakhala mu zoipa,
Chifukwa ndinachimwa.

Mmene ndafika
kwa ‘tate,
Nandikonzeratu phwando;
“Tidye tisekere naye,
Mwanayu anasowa.”

Koma mkulu wanga ndiye,
Sanandirandiretu;
Sanafune tate wanga,
Andikhululukire.

Ambuye amayitana,
Anthu onse ochimwa;
Kuti adzetu kwa Iye,
Kumene kuli moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
Next: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version