Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

  1. Home   »  
  2. Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

 

AMBUYE’naitan’ne;
“Dzapumulire kuno,
Tsamira mutu, mwana’we
M’chifuwa mwanga muno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo;
Wolema, wachisoni;
Anandipulumutsako,
Nakondweretsa ine.

Ambuye naitana’ne;
“Ndipatsa anthu madzi,
Wotopa ndi waludzu’we
Dzamwere moyo kuno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo.
Ndamwera madzi awa;
Laleka ndithu ludzulo,
Tsopano moyo wadza

Ambuye naitana’ne;
“La dziko ndine Dzuŵa,
Yang’ana Ine, kwacha’we,
Wachoka mdima uja.”

Ndayang’anira Mbuyeyo
Ndzapeza Dzuŵa langa
Londiyendetsa bwinoli
Pa njira yanga yonse.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version