Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

 

AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Nanga inu? Nanga inu?
Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?

Masiku onse timakondwera
Pakumva Mawu ake a Yesu;
Wolalikira tidzamumvera;
Nanga inu?

Ife tiyembekezera YESU,
Nanga inu? Nanga inu?
Chimwemwecho chilimumtimamu;
Nanga inu?

Titasokera tinabwerera,
Nanga inu? Nanga inu?
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo;
Nanga inu?

Tinachoka munjira ya imfa,
Nanga inu? Nanga inu?
Takopeka ndi Mawu a Yesu;
Nanga inu?

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version