Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

 

PENYETSETSA Yesu,
Mtima wosauka; Anafera iwe,
Idza, nupumule.
Iye anachotsa
Nsoni ndi zoipa;
Penyetsetsa Yesu,
Ndi kukhulupira.

Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa;
Yachuluka ntchito,
Mphamvu idzakula.
Akonzera kwawo
Nyumba zokhalamo;
Penyetsetsa Yesu,
Mtsatetu tsopano.

Penyetsetsa Yesu
Pogwirana nawo;
Nkhondo ikabvuta
Tamva Mbuye wako.
Achuluka’dani,
Iwe ungofoka;
Penyetsetsa Yesu,
Mantha adzachoka.

Ndipo pakuloŵa
M’dziko la Kumwamba,
Udzapeza komwe
Onse adzatama.
Mwa zoŵala zija
Za Kumwamba kwawo,
Udzapenya maso
Yesu Mbuye wako.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version