Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version