Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

  1. Home   »  
  2. Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

 

KONZA mtima iwe mbale,
Pakuleka tchimo;
Siya zonse uzikonda,
Ndikutsata Yesu.

Konza mtima wako lero,
Yesu alowemo;
Ndipo usachedwe iwe,
Taata Yesu lero.

Imva kuyankhula kwake,
Mawu a chikondi;
Ayankhula iwe lero,
Kuti upumule.

Nthawi ya chisomo m’dziko,
Ndi inotu mbale;
Yom’dziwatu Mpulumutsi,
Ukali ndi moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 514 Osanatu, osana,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version