Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 113 KALERO anthu onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 113 KALERO anthu onse

Hymn 113 KALERO anthu onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 113 KALERO anthu onse

 

KALERO anthu onse
Nachimwa kwa Mulungu
Mulungu anawona
Nawona tchimo lawo,
Nafuna kwawononga,
Nafuna kwawononga.

Mulungu anatuma,
Natuma mvula ija,
Nadzaza dziko lonse
Anafa anthu onse,
Anafa m’mvula muja,
Anafa m’mvula muja.

Mulungu anatuma,
Natuma Nowa uja,
Wamanga chombo chake,
Ndi chachitalitali,
Nowayo nayendamo,
Nowayo nayendamo.

Nowayo anatuma,
Natuma chikwangwala,
Chatsika pansi pansi,
Chosabwerera konse,
Chithaŵa m’talitali,
Chithaŵa m’talitali.

Kutuma wabwereza,
Natuma nkhunda ija,
Yatsika pamadzipo,
Yathyolatu mayani,
Yampatsa Nowa yemwe,
Yampatsa Nowa yemwe.

Kalelo Mbuye Yesu
’Nafera anthu onse,
Ndiyeyo chombo chathu,
Tikabisala mommo
Tipulumuka mommo,
Tipulumuka mommo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version