Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

  1. Home   »  
  2. Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

 

MUBWERE Mzimu Inu
Woyera, wakufatsa,
Muchotse mdima m’mtima mwathu
Tikapenye m’maso.

Mtisangalatse m’zonse,
Ndi wachifundo Inu,
Tiyembekeze kumapazi
A Mbuyathu Yesu.

Mtitsitsimutse ife
Kuchotsa nkhaŵa zathu,
Muyatse moto wachikondi
Mu mitima yathu.

Mtitsutse titachimwa
kutilapitsa m’mtima,
Mwonetsenso chikondi chokhululukira tchimo.

Kutiyeretsa m’mtima
Ndi ntchito yanu yokha,
Kupatsa moyo watsopano
M’mene timafoka.

Mukhale m’kati mwathu,
Mutichotsere mantha,
Tidzayamika ’Tate wathu,
Mwana wawo ndi ’Nu.

Post navigation

Previous: Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Next: Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version