Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

  1. Home   »  
  2. Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

 

MUBWERE Mzimu Inu
Woyera, wakufatsa,
Muchotse mdima m’mtima mwathu
Tikapenye m’maso.

Mtisangalatse m’zonse,
Ndi wachifundo Inu,
Tiyembekeze kumapazi
A Mbuyathu Yesu.

Mtitsitsimutse ife
Kuchotsa nkhaŵa zathu,
Muyatse moto wachikondi
Mu mitima yathu.

Mtitsutse titachimwa
kutilapitsa m’mtima,
Mwonetsenso chikondi chokhululukira tchimo.

Kutiyeretsa m’mtima
Ndi ntchito yanu yokha,
Kupatsa moyo watsopano
M’mene timafoka.

Mukhale m’kati mwathu,
Mutichotsere mantha,
Tidzayamika ’Tate wathu,
Mwana wawo ndi ’Nu.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version