Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

 

MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
Mufike nazo mphamvu zanu zazikuluzo.

Mufike monga nyali younika m’mtimamo.
Mutidziŵitse zakuipa zakukhalamo.

Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
Mutiyeretse ifetu m’mitima mwathumo.

Mufike monga ngati njiŵa yamtenderewo.
Kutitu anthu anu onse akondanetu.

Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
Tikhale tonse nazo mphamvu zanu zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version