Chichewa Christian Hymns
Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Kuyatsa moto m’mtima mwathu;
Ntchito ndi yanu kudzozera
Ndi kutininkha mphatsozo.
Kudzodza kwanu kutipatsa
Chimwemwe, moyo ndi mtendere;
Kuŵala kwanu kupenyetsa
A m’mdima ndi a m’ndendemo.
Mtima wodetsa mukonzere,
Chisomo chanu chakwanira;
Adani athu muthaŵitse
Mutidziŵitse ‘Tate wathu,
Ndi mwana wake ndinu Mmodzi.
Mnafuma kwa aŵiri onse,
Koma Mulungu Mmodziyo