Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

 

MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Kuyatsa moto m’mtima mwathu;
Ntchito ndi yanu kudzozera
Ndi kutininkha mphatsozo.

Kudzodza kwanu kutipatsa
Chimwemwe, moyo ndi mtendere;
Kuŵala kwanu kupenyetsa
A m’mdima ndi a m’ndendemo.

Mtima wodetsa mukonzere,
Chisomo chanu chakwanira;
Adani athu muthaŵitse

Mutidziŵitse ‘Tate wathu,
Ndi mwana wake ndinu Mmodzi.
Mnafuma kwa aŵiri onse,
Koma Mulungu Mmodziyo

Post navigation

Previous: Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version