Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

 

TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
Yakuyamika Mbuye wathuyo;
Mtendere wake tiufunadi,
Titapemphera tinke kwathuko.

Titanka kwathu mkhale nafeko,
Tikufunani Yesu Mbuyathu;
Musunge ife nthaŵi zonsezo,
Mutiyeretse m’mtima mwathu mbuu!

Usiku uno mutisungedi,
Khalani m’fupi m’nyumba mwathumo;
Mamaŵanso mudzatidzutse nji!
Kuti tigwire ntchito zathuzo.

Mtitsogolere nthaŵi zonsezo;
Kuyenda tokha sitikhoza ’yi,
Ngati mukhala Mbuye m’fupimo,
Sitidzaopa kanthu kena ’yi.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version