Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

 

MLUNGU dalitsani Malaŵi,
Mumsunge m’mtendere;
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje;
Lunzitsani mitima yathu
Kuti tisaope,
Mdalitse Mtsogoleri, nafe,
Ndi Mayi Malaŵi.

Malaŵi dziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Ndithudi tadala;
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mphatso zaulere;
Nkhalango, madambo abwino,
Ngwokoma Malaŵi.

O! Ufulu tigwirizane
Kukweza Malaŵi;
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire;
Pankhondo nkana pa mtendere
Cholinga n’chimodzi,
Mayi, Bambo, tidzipereke
Pokweza Malaŵi.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version