Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

 

MLUNGU dalitsani Malaŵi,
Mumsunge m’mtendere;
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje;
Lunzitsani mitima yathu
Kuti tisaope,
Mdalitse Mtsogoleri, nafe,
Ndi Mayi Malaŵi.

Malaŵi dziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Ndithudi tadala;
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mphatso zaulere;
Nkhalango, madambo abwino,
Ngwokoma Malaŵi.

O! Ufulu tigwirizane
Kukweza Malaŵi;
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire;
Pankhondo nkana pa mtendere
Cholinga n’chimodzi,
Mayi, Bambo, tidzipereke
Pokweza Malaŵi.

Post navigation

Previous: Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
Next: Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version