Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 481 USACHIMWE konse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 481 USACHIMWE konse,

Hymn 481 USACHIMWE konse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 481 USACHIMWE konse,

 

USACHIMWE konse,
Lekatu kukwiya;
Uli mwana wake,
Mwana wa Mbuyathu.

Yesu ndi wofatsa,
Yesu ndi woyera;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima

Mzimu wakuipa
Ukusuzumira,
Umakuyesera
Kuti ukachimwe.

Koma usalole
Mawu a Satana;
Bweza tchimo lake,
Chita zolungama.

Yesu ndi Mbuyako,
Mbuyeyo ngwabwino;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version