Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 481 USACHIMWE konse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 481 USACHIMWE konse,

Hymn 481 USACHIMWE konse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 481 USACHIMWE konse,

 

USACHIMWE konse,
Lekatu kukwiya;
Uli mwana wake,
Mwana wa Mbuyathu.

Yesu ndi wofatsa,
Yesu ndi woyera;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima

Mzimu wakuipa
Ukusuzumira,
Umakuyesera
Kuti ukachimwe.

Koma usalole
Mawu a Satana;
Bweza tchimo lake,
Chita zolungama.

Yesu ndi Mbuyako,
Mbuyeyo ngwabwino;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
Next: Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version