Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 692 Paulendo wathu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version