Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 479 ANYAMATA inutu,
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version