Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 479 ANYAMATA inutu,
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version