Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

 

NDIKONDWA kuti
Atate wa M’mwamba,
Atidziwitsa chikondi chakecho;
Ndimaŵerenga m’Uthenga Wabwino,
Kuti Ambuye akonda ana ‘ke.

Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Yesu akonda, andikondabe;
Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Amandikondabe.

Yesu ndim’konda, akondanso ine,
Anandifera pamtanda woopsa;
Wosayenera, woipa ndi
Tsoka langalo Ambuye nachotsa.

Mzimu Woyera akhala mwa ine,
Atsimikiza chikondi cha Yesu:
Ine n’tachimwa amandikumbutsa,
“Lapa mwana we akukonda Yesu.”

Ndikadzawona Ambuye Kumwamba,
Sindidzawopa pokhala akonda:
Anandikonzera kalelo nyumba,
Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version