Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

 

NDIKONDWA kuti
Atate wa M’mwamba,
Atidziwitsa chikondi chakecho;
Ndimaŵerenga m’Uthenga Wabwino,
Kuti Ambuye akonda ana ‘ke.

Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Yesu akonda, andikondabe;
Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Amandikondabe.

Yesu ndim’konda, akondanso ine,
Anandifera pamtanda woopsa;
Wosayenera, woipa ndi
Tsoka langalo Ambuye nachotsa.

Mzimu Woyera akhala mwa ine,
Atsimikiza chikondi cha Yesu:
Ine n’tachimwa amandikumbutsa,
“Lapa mwana we akukonda Yesu.”

Ndikadzawona Ambuye Kumwamba,
Sindidzawopa pokhala akonda:
Anandikonzera kalelo nyumba,
Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.

Post navigation

Previous: Hymn 467 NGOLIZO zilira
Next: Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version