Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,

 

YAMIKANI nonse ’nu,
Pomwimbira nyimbozi
Za masika athuwa;
Potumiza mvulayi,
Mlungu wathu yemwedi
Atipatsa zonsezi;
Timwimbire m’nyumbayi
Za masika athuwa.

Dziko lathu lonseli
Nla Mulungu yemweyu;
Atumiza mphatsozi
Zakutilimbitsadi,
Mmera wathu wonsewu,
Mbewu zathu zonsezi;
Timtamande Mbuyeyu
Wotipatsa zonsezi.

Nthaŵi yina Mbuyeyu
Adzafika pansipa,
Nadzakonza zonsetu;
Zosakondweretsazi
Naziponya m’motowo,
Koma m’nkhokwe mwakemo
Mudzadzala mbewu tho!
Zokomera bwinotu.

’Dzani Mbuye msangatu,
Msonkhanitse zonse phe;
Anthu anu onsewa,
Muwapulumutse ’wo
Zopweteka zawozo,
Ziwathera zonse phe!
’Dzani mu Ufumu ndi,
K’wasonkhanitsa onse.

Post navigation

Previous: Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
Next: Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version