Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

  1. Home   »  
  2. Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

 

M’MAŴA tizifesa
Mbewu zakukoma,
Msana ndi usiku
Tizifesa momwe.
Nyengo yamasika
Tidzatema m’munda,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Ndi zipatsozo
Ndi zipatsozo
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tizifesa m’dzuŵa
Tizifesa m’mthunzi,
Sitiopa ife
Mtambo ndi chisanu.
Athatu masika
Ntchitozi zidzatha;
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tingolira kaya,
Koma tidzafesa
Mbewu za Ambuye;
Ntchitoyo nja Yesu.
Adzachotsa msozi,
Adzatilandira,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Post navigation

Previous: Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
Next: Hymn 444 YEMWE afesa nalira,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version