Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

  1. Home   »  
  2. Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

 

M’MAŴA tizifesa
Mbewu zakukoma,
Msana ndi usiku
Tizifesa momwe.
Nyengo yamasika
Tidzatema m’munda,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Ndi zipatsozo
Ndi zipatsozo
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tizifesa m’dzuŵa
Tizifesa m’mthunzi,
Sitiopa ife
Mtambo ndi chisanu.
Athatu masika
Ntchitozi zidzatha;
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tingolira kaya,
Koma tidzafesa
Mbewu za Ambuye;
Ntchitoyo nja Yesu.
Adzachotsa msozi,
Adzatilandira,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Post navigation

Previous: Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
Next: Hymn 444 YEMWE afesa nalira,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version