Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

 

AKAPANDA kumanga,
Nyumba Yehovayo;
Woyimanga nyumbayo,
Angomanga chabe.

Gwirani ntchito yake,
Ndi mapemphero;
Kuti Yehova adalitse,
Ntchito yanu.

Ngati mugwira ntchito,
Ndi nzeru zanuzo;
Mulibe phindu ndithu,
Pamaso pa Mbuye.

Tipempha ‘Nu Yehova,
M’dalitsetu ntchito;
Zathu kuti Ufumu,
Wanu Ukwezedwe.

Post navigation

Previous: Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
Next: Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version