Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

 

MAWU akewo anamveka ponse,
Olalikidwa ndi aneneriwo;
Kuti yense wakumvera mawuwo,
Apulumuke.

(Mawuwo) Amveke,
(Tu) Kwa onsewo;
(Wo) Muetseratu ‘we sadzafa ndithu.

Tamveratu ‘we Mawu a Mulungu,
Khulupilira mwa
Ambuye Yesu;
Udzalandira moyo wosathawo,
Udzakondwera.

Tsoka kwa iye wosakhulupira,
Zolalikidwa ndi aneneriwo;
Koma patsiku la chiŵeruziro,
Adzafa ndithu

Post navigation

Previous: Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
Next: Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 350 Yesu ati,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version