Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

 

MAWU akewo anamveka ponse,
Olalikidwa ndi aneneriwo;
Kuti yense wakumvera mawuwo,
Apulumuke.

(Mawuwo) Amveke,
(Tu) Kwa onsewo;
(Wo) Muetseratu ‘we sadzafa ndithu.

Tamveratu ‘we Mawu a Mulungu,
Khulupilira mwa
Ambuye Yesu;
Udzalandira moyo wosathawo,
Udzakondwera.

Tsoka kwa iye wosakhulupira,
Zolalikidwa ndi aneneriwo;
Koma patsiku la chiŵeruziro,
Adzafa ndithu

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version