Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 364 DZUŴA lapitira,

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

 

DZUŴA lapitira,
Wadza mdimawo,
Mthunzi wamadzulo
Wagwa m’mwambamo.

M’mwambamo nyenyezi
Zithwanima mbee;
Zonse zili m’tulo
Pansi pali duu.

Yesu mutipatse
Tulo toti phee;
Ndi mdalitso wanu
Mndigonetse ’ne

Mpatse ana ’ng’ono
Alotemo mbee;
Anthu aulendo
Msungesungebe.

Mutonthoze mtima
Wopwetekawo;
Akutsata tchimo
Mletse onsewo.

Wonsewu usiku
Andisunge ’ne
Amithenga anu
Akuyera mbee.

Ndidzukanso m’maŵa,
Kucha koti mbuu,
Ndiyeretu mtima
M’maso mwanumo.

Titamadi ’Tate,
Mwana wakeyo,
Mzimu Woyeranso,
Nthaŵinthaŵizo.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version