Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 364 DZUŴA lapitira,

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

 

DZUŴA lapitira,
Wadza mdimawo,
Mthunzi wamadzulo
Wagwa m’mwambamo.

M’mwambamo nyenyezi
Zithwanima mbee;
Zonse zili m’tulo
Pansi pali duu.

Yesu mutipatse
Tulo toti phee;
Ndi mdalitso wanu
Mndigonetse ’ne

Mpatse ana ’ng’ono
Alotemo mbee;
Anthu aulendo
Msungesungebe.

Mutonthoze mtima
Wopwetekawo;
Akutsata tchimo
Mletse onsewo.

Wonsewu usiku
Andisunge ’ne
Amithenga anu
Akuyera mbee.

Ndidzukanso m’maŵa,
Kucha koti mbuu,
Ndiyeretu mtima
M’maso mwanumo.

Titamadi ’Tate,
Mwana wakeyo,
Mzimu Woyeranso,
Nthaŵinthaŵizo.

Post navigation

Previous: Hymn 363 ATATE ndiyamika,
Next: Hymn 365 DZUŴA lapita,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version