Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

 

MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa;
Ndilibe wina wakundithandiza,
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu.

Kamoyo kanga katha lero lino,
Zidzachokanso zinthuzo za dziko;
Zimasinthika zonse zooneka,
Simusi nthika, mkhale ndinutu.

Koma kalelo mnakhalitsa pano,
Mukhale ndine, msandichokerenso,
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse,
Komatu mukhalitse ndinetu.

E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Usiku, msana, mkhale ndinetu.

Adani sindiopa mukalipo
Muletse tsoka ndi chisoni chino;
Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.

Post navigation

Previous: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
Next: Hymn 363 ATATE ndiyamika,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version