Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

 

MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa;
Ndilibe wina wakundithandiza,
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu.

Kamoyo kanga katha lero lino,
Zidzachokanso zinthuzo za dziko;
Zimasinthika zonse zooneka,
Simusi nthika, mkhale ndinutu.

Koma kalelo mnakhalitsa pano,
Mukhale ndine, msandichokerenso,
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse,
Komatu mukhalitse ndinetu.

E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Usiku, msana, mkhale ndinetu.

Adani sindiopa mukalipo
Muletse tsoka ndi chisoni chino;
Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version