Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

  1. Home   »  
  2. Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

 

PEMPHERO ndiko kufuna,
Kulakalakatu;
Ndi monga moto liyaka
Mumtima wa munthu.

Pemphero ndiko kulira,
Ngakhale misozi,
Kupenyetsetsa Kumwamba,
Mulungu mpafupi.

Pemphero ndiko kufuna
Kwa mwana wamng’ono;
Ndiponso mawu amphamvu
A munthu wamvanu.

Pemphero ndiwo mweyawo
Apuma akristu;
Ndi mapemphero tiloŵa
Dziko la imfalo.

Mutiphunzitse, Mbuyathu,
Kupempha kotero,
Kuyandikira kwa Mlungu
Ndi mtima wabwino.

Post navigation

Previous: Hymn 345 ATATE, ndipempha
Next: Hymn 347 YESU, ndipemphera

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version