Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

  1. Home   »  
  2. Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

 

PEMPHERO ndiko kufuna,
Kulakalakatu;
Ndi monga moto liyaka
Mumtima wa munthu.

Pemphero ndiko kulira,
Ngakhale misozi,
Kupenyetsetsa Kumwamba,
Mulungu mpafupi.

Pemphero ndiko kufuna
Kwa mwana wamng’ono;
Ndiponso mawu amphamvu
A munthu wamvanu.

Pemphero ndiwo mweyawo
Apuma akristu;
Ndi mapemphero tiloŵa
Dziko la imfalo.

Mutiphunzitse, Mbuyathu,
Kupempha kotero,
Kuyandikira kwa Mlungu
Ndi mtima wabwino.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version