Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

 

’TATE wa Kumwambako,
Likayere Dzinalo,
Udzetu Ufumu wanu;
Chifuniro chanucho
Chichitike pansipa
Monga chachitika kwanu.

Mutipatse leroli
E, chakudya chathuchi
Tsiku n’tsiku tichilira.
Mukhululukiredi
Tchimo lathu, monga ’fe
Iwo adatichimwira.

Musatifikitsemo
Muli mayeserowo,
Koma mutipulumutse.
Wanu ndi ufumuwo,
Mphamvu ndi ulemunso
Kufikira nthaŵi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version