Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

 

’TATE wa Kumwambako,
Likayere Dzinalo,
Udzetu Ufumu wanu;
Chifuniro chanucho
Chichitike pansipa
Monga chachitika kwanu.

Mutipatse leroli
E, chakudya chathuchi
Tsiku n’tsiku tichilira.
Mukhululukiredi
Tchimo lathu, monga ’fe
Iwo adatichimwira.

Musatifikitsemo
Muli mayeserowo,
Koma mutipulumutse.
Wanu ndi ufumuwo,
Mphamvu ndi ulemunso
Kufikira nthaŵi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Next: Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version