Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

  1. Home   »  
  2. Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

 

PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Komatu kwa Mulungu kuli
Dziko lakudala;
Mbuyathu Yesu wapitako,
Iye ’natsogola;
Tidzamtsatira ife tonse,
Tsiku lomaliza.

Tiyeni, tiyeni,
Ku dziko lakudala;
Tidzafikira m’dziko ilo
Tsiku lomaliza.

Masiku tikatsala ife
M’dziko mwathu momwe
Mulungu watipatsa ntchito,
Tikazigwiritse.
Pamene zakuipa zathu
Zisautsa ife,
Tikapemphere Mbuye wathu,
Atipulumutse.

Ulendo wathu ukadzatha
Tidzafika kwathu,
Adzatifitsa ife komwe
Yesu Mbuye wathu.
Sitidzapeza masautso
M’dziko la Mulungu,
Tidzakondwera chikondwere
Nthaŵi zathu zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1739 Ife timakufunani

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version