Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

  1. Home   »  
  2. Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

 

PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Komatu kwa Mulungu kuli
Dziko lakudala;
Mbuyathu Yesu wapitako,
Iye ’natsogola;
Tidzamtsatira ife tonse,
Tsiku lomaliza.

Tiyeni, tiyeni,
Ku dziko lakudala;
Tidzafikira m’dziko ilo
Tsiku lomaliza.

Masiku tikatsala ife
M’dziko mwathu momwe
Mulungu watipatsa ntchito,
Tikazigwiritse.
Pamene zakuipa zathu
Zisautsa ife,
Tikapemphere Mbuye wathu,
Atipulumutse.

Ulendo wathu ukadzatha
Tidzafika kwathu,
Adzatifitsa ife komwe
Yesu Mbuye wathu.
Sitidzapeza masautso
M’dziko la Mulungu,
Tidzakondwera chikondwere
Nthaŵi zathu zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Next: Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version