Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

 

KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Kunthawi zosatha;
Komwe kulibe mdima bii,
Yesu ndiye nyaliyo.

Mtandawo tidzasenza,
Korona tidzavala,
Pamodzi ndi oyera,
M’dziko la Kumwambako.

Chikondi chake cha Mlengi wathu,
Natuma Yesuyo;
Kudzatifera tonsefe,
Ndikutipatsa moyo.

Mulitu ulemelero M’mwamba,
Kwa anthu omvera;
Omwe akonda Yesuyo,
Ndikugwira ntchitoyo.

Post navigation

Previous: Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Next: Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version