Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

  1. Home   »  
  2. Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

 

ANA akumwamba ndife,
Paulendo timaimba;
Timatama Mbuye wathu
Wa ulemerero wonse.

Tilikupita kwathu kuja
Munjira ya atate athu,
Amakondwera lero lomwe;
Tinka kuonana nawo.

Mbuye anatiitana
Kukagwira ntchito yake,
Kuitana anthu onse
Atsatenso njira yino.

Inde Mbuye, tibweradi,
Zathu zonse tizisiya,
Mtsogoleri wathu ndinu
Titsatabe inu nokha.

Post navigation

Previous: Hymn 308 AULENDO, munka kuti
Next: Hymn 310 MBUYE munditsogolere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version