Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 308 AULENDO, munka kuti

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

 

AULENDO, munka kuti
Ndi zindodo m’manja mwanu?
Paulendo tizipita;
Aitana Mbuye wathu;
Pamapiri, pamadambo
Tizipita komwe kwawo.
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino,
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino.

Kodi simuopa njira,
Inu anthu akufoka?
Ayi, atiperekeza
Mbuye wathu wotikonda.
Iye amakhala nafe,
Natitsogolera ife.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.

Mundiuze, aulendo,
Muli chiani m’Mwamba muja?
Atibvekako zoyera
Akorona natininkha;
Moyo, moyo atipatsa,
Kwa Mulungu tidzakhala.
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino,
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino.

Kodi inu, aulendo,
Ife titsagane nanu?
Inde, mudze inu nonse,
Mudze nafe paulendo.
Inde, mutiperekeze,
Yesu atilinda ife.
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino,
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version