Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 308 AULENDO, munka kuti

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

 

AULENDO, munka kuti
Ndi zindodo m’manja mwanu?
Paulendo tizipita;
Aitana Mbuye wathu;
Pamapiri, pamadambo
Tizipita komwe kwawo.
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino,
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino.

Kodi simuopa njira,
Inu anthu akufoka?
Ayi, atiperekeza
Mbuye wathu wotikonda.
Iye amakhala nafe,
Natitsogolera ife.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.

Mundiuze, aulendo,
Muli chiani m’Mwamba muja?
Atibvekako zoyera
Akorona natininkha;
Moyo, moyo atipatsa,
Kwa Mulungu tidzakhala.
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino,
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino.

Kodi inu, aulendo,
Ife titsagane nanu?
Inde, mudze inu nonse,
Mudze nafe paulendo.
Inde, mutiperekeze,
Yesu atilinda ife.
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino,
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino.

Post navigation

Previous: Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
Next: Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version