Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

 

AKRISTU limbikani,
Imani mtima nji!
Mbendera nyamulani,
Msatenthemere ’yi.
Wotsogolera wathu
Ndi Mwana wa Mulungu;
Adzagonjetsa onse
Adani athuwo.

Tigwire nkhondo yomwe
Ya Mbuye wathuyo;
Tileke zakuipa
Zokhala m’mtimamo.
Sitikwanira tokha
Kuleka zathu zomwe,
Koma Mbuyathu Yesu
Atithangatatu.

Tsopano timenyana
Ndi zakuipazi;
Pamene nkhondo yatha
Tidzanka kwathuko.
Yesu adzalandira
Ankhondo ake onse;
Adzakhalika naye
Kumwamba komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version