Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

 

ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziŵitsitsa kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Ndine wanu Mbuye wanga,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziwitsitsa
Kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Chifukwa cha dzina lake
Ndanyozedwa ‘ne,
Adani achuluka, ndachepa ine;
Ndiwakonda onse
Koma andisautsa ‘ne,
Pukutani m’maso mwanga misoziyi.

Tiyeni abale tonse
Tilimbe ndithu,
Pogwira ntchito zake
Za Mbuye wathu;
Iye analonjezatu
Tsiku lomaliza,
Tidzakhala muulemelero wake.

Post navigation

Previous: Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
Next: Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hello world!
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version