Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

 

ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziŵitsitsa kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Ndine wanu Mbuye wanga,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziwitsitsa
Kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Chifukwa cha dzina lake
Ndanyozedwa ‘ne,
Adani achuluka, ndachepa ine;
Ndiwakonda onse
Koma andisautsa ‘ne,
Pukutani m’maso mwanga misoziyi.

Tiyeni abale tonse
Tilimbe ndithu,
Pogwira ntchito zake
Za Mbuye wathu;
Iye analonjezatu
Tsiku lomaliza,
Tidzakhala muulemelero wake.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version