Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

 

AMBUYE m’chipululu,
Analefuka ndi njala;
Polowa m’mayesero,
Anagonjetsatu Satana.
M’dziko lapansi lero lino,
Alipo omutsata,
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Nyamulani maso anu,
Muyang’ane m’kati mwanu;
Alipo anthu ena,
Oyitanidwa, nasankhidwa.
Mutawayang’ana iwo,
Akunga a umphawi;
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Kuwachotsa kwa Mbuye,
Satanayo walephera;
Powazunza iwotu,
Achiyesa chimwemwe ndithu.
Ambuye nawalimbikitsa,
Napukuta misozi;
Nawalonjeza koronayo,
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Akhrisitu tilimbike,
Kugwira ntchito ya Mbuye;
Timvere mawu ake,
Tidzagonjetsatu Satana.
Pomalizatu moyo uno,
Tidzapita Kumwamba;
Tidzayimbira Mulunguyo,
Ndife mbewu zosawonongeka.

Post navigation

Previous: Hymn 282 INU muli mehere,
Next: Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version