Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

 

AMBUYE m’chipululu,
Analefuka ndi njala;
Polowa m’mayesero,
Anagonjetsatu Satana.
M’dziko lapansi lero lino,
Alipo omutsata,
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Nyamulani maso anu,
Muyang’ane m’kati mwanu;
Alipo anthu ena,
Oyitanidwa, nasankhidwa.
Mutawayang’ana iwo,
Akunga a umphawi;
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Kuwachotsa kwa Mbuye,
Satanayo walephera;
Powazunza iwotu,
Achiyesa chimwemwe ndithu.
Ambuye nawalimbikitsa,
Napukuta misozi;
Nawalonjeza koronayo,
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Akhrisitu tilimbike,
Kugwira ntchito ya Mbuye;
Timvere mawu ake,
Tidzagonjetsatu Satana.
Pomalizatu moyo uno,
Tidzapita Kumwamba;
Tidzayimbira Mulunguyo,
Ndife mbewu zosawonongeka.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version