Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

 

KHALA chete mtima wanga
Mlungu wako ndiye Mfumu;
Zinthu zonse zisinthika,
Mlungu ndi wachikhalire.

(Khala chete, Chidzakupinga n’chiyani?
Usaope, Mulungu ali nawe.)

Anthu onse pansi pano
Sakhutitsa mtima wawo;
Amadera zinthu zawo,
Namakhumba zakutali.

Khala chete mtima wanga,
Zikwanire zinthu zako;
Usakhumbe zapansipa
Koma Mlungu wako yekha.

Post navigation

Previous: Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
Next: Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version