Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 238 MULUNGU wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 238 MULUNGU wanga,

Hymn 238 MULUNGU wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 238 MULUNGU wanga,

 

MULUNGU wanga,
Ndapeza moyo;
Ndili wokondwera
Masiku onse.

Aleluya, muyenera!
Aleluya, Amen.
Aleluya, ndidzamtama
Mulungu wanga.

Mwazi wa Yesu
Unditsukatu,
Ndiye Mbuye wanga
Ndi Mpulumutsi.

Pamtanda wake ’Nafera ine,
Ndi zoipa zanga ’Nazichotsadi.

Mulungu wanga
Andilandira,
Chifukwa cha Yesu
Mwana wakeyo.

Adzabweranso
Kundilandira
Ndikhale ndi Iye
Masiku onse.

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 239 Akumwambawo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version