Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 238 MULUNGU wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 238 MULUNGU wanga,

Hymn 238 MULUNGU wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 238 MULUNGU wanga,

 

MULUNGU wanga,
Ndapeza moyo;
Ndili wokondwera
Masiku onse.

Aleluya, muyenera!
Aleluya, Amen.
Aleluya, ndidzamtama
Mulungu wanga.

Mwazi wa Yesu
Unditsukatu,
Ndiye Mbuye wanga
Ndi Mpulumutsi.

Pamtanda wake ’Nafera ine,
Ndi zoipa zanga ’Nazichotsadi.

Mulungu wanga
Andilandira,
Chifukwa cha Yesu
Mwana wakeyo.

Adzabweranso
Kundilandira
Ndikhale ndi Iye
Masiku onse.

Post navigation

Previous: Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
Next: Hymn 239 TILI ndi mtendere

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version