Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version