Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
Next: Hymn 232 WAFUNAFUNA ine

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version