Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

 

AITANA, aitana dziko lonse,
Imvani mukhaliranji chete?
Aitana,
Aitana aitana dziko lonse.

Mfumu iyi, Mfumu iyi ya Kumwamba
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa anthu onse.
Anthu onse, anthu onse, tinke kwawo.

Aitana,aitana inu mayi,
Ndi Yesu, amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu mayi.

Aitana, aitana inu ’tate,
Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu ’tate.

Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
Zoipa zimene muzichita, muzisiye,
Muzisiye, muzisiye inu nonse.”

Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
Ndi Yesu anatifera ife akuchimwa;
Akuchimwa, akuchimwa tinke kwawo.

Post navigation

Previous: Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
Next: Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version