Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

 

AITANA, aitana dziko lonse,
Imvani mukhaliranji chete?
Aitana,
Aitana aitana dziko lonse.

Mfumu iyi, Mfumu iyi ya Kumwamba
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa anthu onse.
Anthu onse, anthu onse, tinke kwawo.

Aitana,aitana inu mayi,
Ndi Yesu, amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu mayi.

Aitana, aitana inu ’tate,
Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu ’tate.

Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
Zoipa zimene muzichita, muzisiye,
Muzisiye, muzisiye inu nonse.”

Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
Ndi Yesu anatifera ife akuchimwa;
Akuchimwa, akuchimwa tinke kwawo.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hello world!
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version