Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

 

LERO lino mbale wanga,
Ndilo tsiku lakukoma;
Talandira Mpulumutsi,
Mmene ali kuyitana.

Lero lino mbale wanga,
Usazengereze ayi;
Ngati ulandira Yesu,
Lero, udzachita mwayi.

Lero lino ndi labwino,
Moyo wako uli nawo;
Pena mawa umwalira,
Udzatani mlandu wako?

Lero lino mbale wanga,
Lapa mtima, lapa tchimo;
Yesu adzakulandira,
Ukam’pempha lero lino.

Ndiwe mlendo lero lino,
Myera ndikupempha iwe:
Yesu Mwana wa Mulungu,
Akufuna ndithu iwe.

Inde, lero lino Yesu,
Ayitana inu nonse;
Landirani Mpulumutsi,
Musazengereze konse.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version