Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

 

LERO lino mbale wanga,
Ndilo tsiku lakukoma;
Talandira Mpulumutsi,
Mmene ali kuyitana.

Lero lino mbale wanga,
Usazengereze ayi;
Ngati ulandira Yesu,
Lero, udzachita mwayi.

Lero lino ndi labwino,
Moyo wako uli nawo;
Pena mawa umwalira,
Udzatani mlandu wako?

Lero lino mbale wanga,
Lapa mtima, lapa tchimo;
Yesu adzakulandira,
Ukam’pempha lero lino.

Ndiwe mlendo lero lino,
Myera ndikupempha iwe:
Yesu Mwana wa Mulungu,
Akufuna ndithu iwe.

Inde, lero lino Yesu,
Ayitana inu nonse;
Landirani Mpulumutsi,
Musazengereze konse.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 121 Imbira!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version