Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

 

SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
Pali anthu otayika, masiku alikutha;
Ngati tikondwerera,
Pakuyenda ulendowu,
Tonse tidzachita bwino, masiku alikutha.

Akutha, akutha, masiku akutha,
Tonse tichitetu bwino, masiku ali kutha.

Tisakhale awulesi, masiku alikutha,
Nkhope zathu zikondwere, masiku alikutha;
Dziko ili ndi lochimwa, lodzaza ndi chisoni,
Thangatani akugwawo, masiku alikutha.

Tamangidwa ndi unyolo, masiku alikutha,
Tisiyetu zoipazi, masiku alikutha;
Tonsefe muzabwinotu
Tidzakhala ndi Mlungu;
Ndipo tidzakondweradi mu nthawi zamuyaya,

Post navigation

Previous: Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
Next: Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hello world!
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version