Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

 

SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
Pali anthu otayika, masiku alikutha;
Ngati tikondwerera,
Pakuyenda ulendowu,
Tonse tidzachita bwino, masiku alikutha.

Akutha, akutha, masiku akutha,
Tonse tichitetu bwino, masiku ali kutha.

Tisakhale awulesi, masiku alikutha,
Nkhope zathu zikondwere, masiku alikutha;
Dziko ili ndi lochimwa, lodzaza ndi chisoni,
Thangatani akugwawo, masiku alikutha.

Tamangidwa ndi unyolo, masiku alikutha,
Tisiyetu zoipazi, masiku alikutha;
Tonsefe muzabwinotu
Tidzakhala ndi Mlungu;
Ndipo tidzakondweradi mu nthawi zamuyaya,

Post navigation

Previous: Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
Next: Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version