Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

 

ANTHU m’maiko onse
Akhala mitundu;
Kapena m’dziko lino
Akhala anzathu;
Agona mwa zoipa,
Apulukiradi,

Ati, Mutilangize
Abale, bwerani.

Ngakhale alemera
Ndi chuma cha dziko,
Kodi akakondwera
Opanda Mulungu?
Kodi akhala mwaŵi
Otsata zawozo?
Iyai, awonongeka,
Apeza tsokalo.

Ndi ife akudziŵa
Chikondi cha Mlungu,
Kodi tidzaŵamana
Kuŵala kwa Kristu?
Chipulumutso! Inde,
Tichibukitsetu,
Kuti mitundu yonse
Ibwere kwa Yesu.

Akristu nyamulani
Maneno a Mulunguyo,
Ndi moyo lalikani
Pa dziko lonselo;
Ndi Yesu Mpulumutsi
Anatiferatu;
Adzabvomera onse;
Ndi Mwana wa Mlungu.

Post navigation

Previous: Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
Next: Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version