Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

 

ANTHU m’maiko onse
Akhala mitundu;
Kapena m’dziko lino
Akhala anzathu;
Agona mwa zoipa,
Apulukiradi,

Ati, Mutilangize
Abale, bwerani.

Ngakhale alemera
Ndi chuma cha dziko,
Kodi akakondwera
Opanda Mulungu?
Kodi akhala mwaŵi
Otsata zawozo?
Iyai, awonongeka,
Apeza tsokalo.

Ndi ife akudziŵa
Chikondi cha Mlungu,
Kodi tidzaŵamana
Kuŵala kwa Kristu?
Chipulumutso! Inde,
Tichibukitsetu,
Kuti mitundu yonse
Ibwere kwa Yesu.

Akristu nyamulani
Maneno a Mulunguyo,
Ndi moyo lalikani
Pa dziko lonselo;
Ndi Yesu Mpulumutsi
Anatiferatu;
Adzabvomera onse;
Ndi Mwana wa Mlungu.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version