Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

 

MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Ndi kundidzaza moyo wanuwo,
Kuti ndikonde zomwe mukondanso,
Ndichite chomwe mumachitanso.

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Mpaka mtimanga ukayeretu,
Ndipo zokhumba zanga zilingane
Nazo zanuzo zakuyera mbuu!

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Mpaka ndikhale wanu nokhatu;
Ayeretsedwe makhalidwe anga
Ndi mphamvu yanu yondisunga nji!

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Kuti inedi ndisafe ’yitu,
Koma ndikhale nanu m’moyo womwe
Wangwiro ndi wa nthaŵi zonsetu.

Post navigation

Previous: Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
Next: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version