Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

 

DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
Ndili ndekha mpanjira n’kwaŵenitu;
Ndilibetu chakudya, ndilibetu chakumwa,
Ndingoyenda mpanjira n’kwaŵenitu.

N’kwawenitu,
N’kwawenitu,
Dziko lino sikwathu
N’kwaŵenitu.

Dziko lino lapansi mavuto ndi osatha,
Ine sindingalithe n’kwaŵenitu;
Ukasowa chumacho, abwenzi akuthawa,
Koma kwathu satero n’kwaŵenitu.

Anyamata, ‘sungwana
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu;
Abambo ndi amayi
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu.

Tiyeni abale ‘fe tiyang’ane kwa Yesu,
Yemwe angatipatse moyowotu;
Moyo uno wam’dziko abale ndi wozunza,
Moyo wokoma ndiwo wa Yesuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hello world!
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version