Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

 

LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
Tamvani nyimbo za ‘mithenga aKumwambako;
Nafenso pansipa
Tim’yamikire ’Ye,
Ndi Mpulumutsi wathu wotifera kalero.

Lambira Yesuyo,
Wokonda tonsefe;
Mabala ake achikondi awonekabe;
Tisayiwale ’yi
Zoŵaŵa zakezo,
Tileke kum’chimwira, kum’sautsa Yesuyo.

Lambira Yesuyo,
Uthenga wakewu
Uyanjanitsa anthu onse m’dziko munomo:
Amaiŵala za
Kudana kwawoko,
Nayamikira Mfumu yamtendere monsemo.

Lambira Mfumuyo
Wolenga zonsezi:
Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi mitamboyi;
Tikweze dzinalo
La Mbuye Yesuyo,
Tim’yamikire pansi pano ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
Next: Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version