Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

 

LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
Tamvani nyimbo za ‘mithenga aKumwambako;
Nafenso pansipa
Tim’yamikire ’Ye,
Ndi Mpulumutsi wathu wotifera kalero.

Lambira Yesuyo,
Wokonda tonsefe;
Mabala ake achikondi awonekabe;
Tisayiwale ’yi
Zoŵaŵa zakezo,
Tileke kum’chimwira, kum’sautsa Yesuyo.

Lambira Yesuyo,
Uthenga wakewu
Uyanjanitsa anthu onse m’dziko munomo:
Amaiŵala za
Kudana kwawoko,
Nayamikira Mfumu yamtendere monsemo.

Lambira Mfumuyo
Wolenga zonsezi:
Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi mitamboyi;
Tikweze dzinalo
La Mbuye Yesuyo,
Tim’yamikire pansi pano ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version