Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

  1. Home   »  
  2. Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

 

TIYENI, dzalireni nane,
Tidze ku mtanda wa Ambuye,
Tionse tichitetu maliro;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Kodi misozi itisoŵa,
Poona anthu amanyoza?
Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Anena mawu m’mtanda momwe
Mawu ochepa achifundo,
Apempherera ’dani ake;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Mtima wangawe, uyenera
Kuduka ndi manyazi lero,
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Ona chikondi cha Mulungu,
Ona zoipazo za anthu,
Koma chakula ndi chikondi;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Post navigation

Previous: Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
Next: Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version