Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

  1. Home   »  
  2. Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

 

TIYENI, dzalireni nane,
Tidze ku mtanda wa Ambuye,
Tionse tichitetu maliro;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Kodi misozi itisoŵa,
Poona anthu amanyoza?
Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Anena mawu m’mtanda momwe
Mawu ochepa achifundo,
Apempherera ’dani ake;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Mtima wangawe, uyenera
Kuduka ndi manyazi lero,
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Ona chikondi cha Mulungu,
Ona zoipazo za anthu,
Koma chakula ndi chikondi;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version