Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

  1. Home   »  
  2. Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

 

TIIMBE nyimbo zotamanda
Mulungu wathu wabwino,
Pakuti akondana nawo
Anthu okhala padziko;
Tero natuma Mwana wake,
Wakukondedwa kalelo,
Kutiphunzitsa ife tonse
Za chikondano chakecho.

Mulungu ndiye wachifundo,
Nadzalandira onsewa
Akuulula mphulupulu
Ndi kukondana ndi Yesu
Tilondelonde njira yake
Yopapatiza yaing’ono;
Adzatilondolera ndiye
Kutifikitsa m’Mwambamo.

Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Dzanja Mbuyathu agwira;
Tikadagwira ntchito zake
Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
Pena misozi maliro;
Mulungu tidzamtamandira,
Inde kosalekezanso.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 510 Ngolizo zilira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version