Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

 

MU ZONSE abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa anthu ake,
Zomwe iwo akuzisowa.

Akhrisitu pamavuto tiyeni timulemekeze,
Pamtendere tiyeni timulemekeze.
Maso ake ali pa anthu,
Okhala m’dziko lapansi.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kuveka anthu ake,
Ngakhale nyama zakuthengo.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa mphatso zake,
Ngakhalenso kwa tiŵanato.

Post navigation

Previous: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Next: Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version