Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

 

MU ZONSE abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa anthu ake,
Zomwe iwo akuzisowa.

Akhrisitu pamavuto tiyeni timulemekeze,
Pamtendere tiyeni timulemekeze.
Maso ake ali pa anthu,
Okhala m’dziko lapansi.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kuveka anthu ake,
Ngakhale nyama zakuthengo.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa mphatso zake,
Ngakhalenso kwa tiŵanato.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version