Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

  1. Home   »  
  2. Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

 

INU Mulungu, tikuyamikani;
Tivomereza ndinu Ambuyathu;
Ponse, atate, akugwadirani,

Nanu akukuzani amithenga,
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu zake,
Nanu angelo a mitundu yonse
Akuimbirani:

“Mbuye Woyera! E, Woyera nokha!
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu!
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza;
Pansi ndi Kumwamba.”

Inu atumwi akumweka aja,
Ndi aneneri oyanjana omwe;
Ndi aunyinji anakuferani;
Akuyamikani.

Mpingo Woyera! wa kwa anthu onse;
Ukumverani, Mfumu ndi Atate,
Mwana woona wa ulemu wonse,
Mzimu, Nkhoswe yemwe.

Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mwana wosatha wa Atate ndinu!
Simunanyoza mimba ya Namwali;
Potipulumutsa.

Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
Njira munatsegula tikaloŵe;
Momwe mukhala Inu ndi Atate;
Mu ulemerero

Kumva milandu yathu mudzabwera;
Mutithandize, atumiki anu;
Mwatiwombola nawo mwazi wanu;
Mutipulumutse.

M’tiŵerengere
M’Mwamba ndi oyera;
Mutidalitse, ndi’fe anthu anu;
Moyo wosatha, mutipatse tonse;
Mutilamulire.

Tsiku ndi Tsiku timalemekeza;
Nanu tikukuzani osaleka;
Mbuye, m’tisunge tingachimwe lero;
M’tichitire nsisi.

Mbuye, chifundo chanu chitigwere;
Monga tikhulupi’ra inu nokha;
Takhulupi’ra zedi mwa’Nu, Mbuye;
Tisagome konse!

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version