Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

  1. Home   »  
  2. Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

 

INU Mulungu, tikuyamikani;
Tivomereza ndinu Ambuyathu;
Ponse, atate, akugwadirani,

Nanu akukuzani amithenga,
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu zake,
Nanu angelo a mitundu yonse
Akuimbirani:

“Mbuye Woyera! E, Woyera nokha!
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu!
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza;
Pansi ndi Kumwamba.”

Inu atumwi akumweka aja,
Ndi aneneri oyanjana omwe;
Ndi aunyinji anakuferani;
Akuyamikani.

Mpingo Woyera! wa kwa anthu onse;
Ukumverani, Mfumu ndi Atate,
Mwana woona wa ulemu wonse,
Mzimu, Nkhoswe yemwe.

Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mwana wosatha wa Atate ndinu!
Simunanyoza mimba ya Namwali;
Potipulumutsa.

Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
Njira munatsegula tikaloŵe;
Momwe mukhala Inu ndi Atate;
Mu ulemerero

Kumva milandu yathu mudzabwera;
Mutithandize, atumiki anu;
Mwatiwombola nawo mwazi wanu;
Mutipulumutse.

M’tiŵerengere
M’Mwamba ndi oyera;
Mutidalitse, ndi’fe anthu anu;
Moyo wosatha, mutipatse tonse;
Mutilamulire.

Tsiku ndi Tsiku timalemekeza;
Nanu tikukuzani osaleka;
Mbuye, m’tisunge tingachimwe lero;
M’tichitire nsisi.

Mbuye, chifundo chanu chitigwere;
Monga tikhulupi’ra inu nokha;
Takhulupi’ra zedi mwa’Nu, Mbuye;
Tisagome konse!

Post navigation

Previous: Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
Next: Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version