Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

 

KONDA dzinalo la Yesu,
Mwana wosawuka’we;
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.

Dzina la Yesuyo,
N’lokondwetsa onsewo;
M’mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.

Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwako monsemo;
Mmene ulikuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.

Dzina ili ndi lokoma,
La Mtetezi wathuyo;
Mmene adzatilandira,
M’mwamba tidzakondwadi.

Mbuye Yesu tim’tamanda,
Ndi nyimbo zathu zonse;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version