Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

 

YANG’ANANI, anthu onse,
Yesu Mbuye wathuyo:
Alinkudza ndi ulemu,
Kuoneka m’Mwambamo.

Anthu onse am’lambire
Yesu Mwana wa Mulungu
Alinkudza ndi ulemu
Wopambana, indetu.

Adzatenga anthu ake
Akumvera pansipo
Iwo adzakhala naye
M’dziko la Kumwambako.

Koma anthu onse omwe
Anamnyoza pansipo,
Nthaŵi Yesu alinkudza
Adzaopa m’mtimamo.

Ife tonse tikumbuke
Mawu ake onsewo;
Timuyang’anire Iye,
Yesu Mbuye wathuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
Next: Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version