Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

 

YANG’ANANI, anthu onse,
Yesu Mbuye wathuyo:
Alinkudza ndi ulemu,
Kuoneka m’Mwambamo.

Anthu onse am’lambire
Yesu Mwana wa Mulungu
Alinkudza ndi ulemu
Wopambana, indetu.

Adzatenga anthu ake
Akumvera pansipo
Iwo adzakhala naye
M’dziko la Kumwambako.

Koma anthu onse omwe
Anamnyoza pansipo,
Nthaŵi Yesu alinkudza
Adzaopa m’mtimamo.

Ife tonse tikumbuke
Mawu ake onsewo;
Timuyang’anire Iye,
Yesu Mbuye wathuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version