Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

 

MLUNGU dalitsani Malaŵi,
Mumsunge m’mtendere;
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje;
Lunzitsani mitima yathu
Kuti tisaope,
Mdalitse Mtsogoleri, nafe,
Ndi Mayi Malaŵi.

Malaŵi dziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Ndithudi tadala;
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mphatso zaulere;
Nkhalango, madambo abwino,
Ngwokoma Malaŵi.

O! Ufulu tigwirizane
Kukweza Malaŵi;
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire;
Pankhondo nkana pa mtendere
Cholinga n’chimodzi,
Mayi, Bambo, tidzipereke
Pokweza Malaŵi.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version