Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

  1. Home   »  
  2. Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

 

TIIMBE ndi kulalikira
Mthenga wa chikondicho
Anamva Mlungu m’Mwambamo
Kulira kwathu pansipa.

(Ndikhulupirira Yesu
Wobadwira m’kholamo;
Iye ndiye Mfumu yathu,
Timtame nthaŵi zonse.)

Kwa ife lero anabadwa
Mwana wa Mariyayo,
Pamsinkhu, ine mng’ono koma
Mwini dziko lonseli.

Anadza nazo mphatso zake
Anatikonzeratu; Anatitseguliradi
Pakhome pa Ufumuwo.

Ambuye takutamandani
Tsiku lakubadwali,
Mwa Inu tonse tikondwera,
Tiseke tonsefe.

A! Yesu Mbuye wakuyera,
Munagona m’kholamo;
Mudzikonzere leronso
Mogona m’mtima mwangamu.

Ulemerero m’Mwambamwamba
Ndi mtendere pansipa;
Tiimbe nafe nyimboyi,
Timyamikire Mbuyathu

(Yesu ndiye Mfumu,
Yesu ndiye Mfumu!
Ndikhulupirira Yesu wobadwira m’kholamo.)

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version