Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

  1. Home   »  
  2. Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

 

TIIMBE ndi kulalikira
Mthenga wa chikondicho
Anamva Mlungu m’Mwambamo
Kulira kwathu pansipa.

(Ndikhulupirira Yesu
Wobadwira m’kholamo;
Iye ndiye Mfumu yathu,
Timtame nthaŵi zonse.)

Kwa ife lero anabadwa
Mwana wa Mariyayo,
Pamsinkhu, ine mng’ono koma
Mwini dziko lonseli.

Anadza nazo mphatso zake
Anatikonzeratu; Anatitseguliradi
Pakhome pa Ufumuwo.

Ambuye takutamandani
Tsiku lakubadwali,
Mwa Inu tonse tikondwera,
Tiseke tonsefe.

A! Yesu Mbuye wakuyera,
Munagona m’kholamo;
Mudzikonzere leronso
Mogona m’mtima mwangamu.

Ulemerero m’Mwambamwamba
Ndi mtendere pansipa;
Tiimbe nafe nyimboyi,
Timyamikire Mbuyathu

(Yesu ndiye Mfumu,
Yesu ndiye Mfumu!
Ndikhulupirira Yesu wobadwira m’kholamo.)

Post navigation

Previous: Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
Next: Hymn 456 ANA inu, ana inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version