Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

 

OYAMIKA Mlungu m’bwere,
Zamasika mudzayimbe;
Dzinthu dzathu takolola,
Sidzionongeka m’minda.
Mlungu Mlengi asamala,
Zotisowa akonzera;
M’lowe m’nyumba ya Chauta.
M’kweze nyimbo zamasika.

Dziko lonse n’la Mulungu,
Kuti lim’balire dzinthu;
M’munda zonse zimamera,
Zakukoma ndi zoipa.
Mmera udza, bwino ngala,
Maso omwe amakhwima;
Mutilole, mwini dzinthu,
Tikakhale dzinthu dzanu.

Adzabwera Mbuye wathu,
Kukolola dzinthu dzake;
M’munda mwake akachotse,
Minga ndi zoipa zonse.
Adzatumanso angelo,
Minga akaponye m’moto;
Koma tirigu amsunge,
M’nkhokwe yake nthawi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version